• Friday June, 2025

Archangel Nzangaya

Archangel Nzangaya

Articles by Archangel Nzangaya

UDF Delays Next Week’s Elective Convention
Malawi News

UDF Delays Next Week’s Elective Convention

The United Democratic Front (UDF) has postponed its National Elective Conference, originally scheduled for August 3, 2024. UDF Acting Publicity Secretary Yusuf Mwawa, through a statement, announced that the party's National Executive Committee decided to… ...

Nzika ya ku Britain yabedwa ku Lilongwe
Malawi News

Nzika ya ku Britain yabedwa ku Lilongwe

Apolisi munzinda wa Lilongwe atsimikiza kuti nzika ya m’dziko la Britain ya zaka 26 yabedwa ndi anthu osadziwika pomwe imachokera ku mapemphero Lolemba masana.  Malingana ndi ofalitsa nkhani za polisi ya Lilongwe a Hastings Chigalu,… ...

Dziko lapita kwa agalu – watelo Kalindo
Malawi News

Dziko lapita kwa agalu – watelo Kalindo

Omenyera ufulu wa anthu Bon Kalindo yemwe wavekedwa unyolo mowilikiza pakatipa wati zithu zambiri ndizosokonekera m'dziko muno kamba koti dziko lino linapita kwa agalu. Poyankhula mu pologalamu ya padera yomwe yaulutsidwa pa wayilesi ya Zodiak… ...

Abale sakudziwabe komwe kuli Chiyanjano Mbeza
Malawi News

Abale sakudziwabe komwe kuli Chiyanjano Mbeza

Patadutsa maola oposa 24 apolisi chimangileni mkozi wa nyimbo, Chiyanjano Mbeza pa mlandu omwe sukudziwika, achibale ake ati mpaka pano sakudziwabe polisi yomwe m'bale wawoyu akusungidwa. Mbeza yemwe amajambula nyimbo munzinda wa Blantyre, anamangidwa madzulo… ...

Lekani kuononga misonkho pomayenda m’misika, tsitsani mitengo ya zinthu – wadzudzura Mneneri David Mbewe
Malawi News

Lekani kuononga misonkho pomayenda m’misika, tsitsani mitengo ya zinthu – wadzudzura Mneneri David Mbewe

Mtsogoleri wa chipani cha Liberation for Economic Freedom (LEF) M'neneri David Mbewe, wauza wachiwiri kwa mtsogoleri wa dziko lino Michael Usi kuti asiye kuyendera misika ponena kuti akuononga misonkho yomwe itha kugwira ntchito zina zotukura… ...

Malawi exceeds blood collection target
Malawi News

Malawi exceeds blood collection target

The Malawi Blood Transfusion Service (MBTS) has disclosed that blood donation has significantly increased in the country to an extent where it has surpassed the collection target. This is according to the MBTS Acting Chief… ...

Aliyese ali ndi ufulu osintha chipani – yatelo DPP
Malawi News

Aliyese ali ndi ufulu osintha chipani – yatelo DPP

Chipani chotsutsa boma cha Democratic Progressive (DPP) chatsimikiza za kutuluka m’chipani kwa a Dalitso Kabambe, koma chati sichikudandaula ponena kuti ngakhale banja limene limatha ndipo aliyese amalowera kwake. Potsatira kalata yomwe a Kabambe omwe anakhalaposo… ...

Bullets president Buckle challenges players to bring results
Malawi News

Bullets president Buckle challenges players to bring results

After addressing their concerns, FCB Nyasa Big Bullets president, Konrad Buckle, has issued a call to the players to demonstrate resilience and commitment to the team's emblematic cause. A week after the players abstained from… ...

Teacher at large after defiling 13-year-old learner
Malawi News

Teacher at large after defiling 13-year-old learner

Police in Chiradzulu are hunting for a teacher at Maravi Primary School in Chiradzulu for allegedly defiling a 13-year-old learner. Chiradzulu police public relations officer has identified the teacher as Chimwemwe Chitani who defiled the… ...

Thupi la Lucius Banda lifika m’dziko muno masanawa
Malawi News

Thupi la Lucius Banda lifika m’dziko muno masanawa

Thupi la katswiri pa mayimbidwe, Lucius Banda, likuyembekezeka kufika m’dziko muno lero masanawa kuchokera m'dziko la South Africa komwe wamwalilira, ndipo pali chiyembekezo kuti lilowa m’manda Lachinayi sabata ino. Izi ndi malingana ndi mwana wa… ...