Opikisana 13 pa President ku Malawi ndi chibwana chabe – Chaima
M'modzi mwa akatswiri ozukutapo pa ndale a George Chaima ati m'mene dziko la Malawi lilili nkukhala ndi atsogoleri mpaka khumi ndi atatu (13) okapikisana pa mpando wa utsogoleri wa dziko ndi chibwana chabe chomwe Malawi… ...