• Saturday February, 2025

Mphatso Khutcha Richard

Mphatso Khutcha Richard

Articles by Mphatso Khutcha Richard

Makhonsolo alibe ndalama – Ngwale
Malawi News

Makhonsolo alibe ndalama – Ngwale

Phungu wa ku Nyumba ya Malamulo dera la Chiradzulu West Mathews Ngwale, wadandaula kuti aphungu akayima kupempha zitukuko ku ma unduna, unduna ukakhala opanda mayankho umawabwezera nkhani ya chitukukocho kuti aphungu apite nayo ku khonsolo… ...

Anthu ena akufuna ine ndi a Chakwera tiyambane – Usi
Malawi News

Anthu ena akufuna ine ndi a Chakwera tiyambane – Usi

A Michael Usi omwe ndi wachiwiri kwa mtsogoleri wa dziko lino ati pali anthu ena amene akuyesetsa kuti iwo ndi mtsogoleri wa dziko lino a Lazarus Chakwera ayambane ndipo ati khalidwe lotelo limazunzitsa aMalawi, pamene… ...

Pepani aMalawi, a Chakwera anakutaitsani nthawi – Chaponda
Malawi News

Pepani aMalawi, a Chakwera anakutaitsani nthawi – Chaponda

A George Chaponda mtsogoleri wa mbali yotsutsa boma mnyumba ya malamulo, ati akupepesa onse amene anabwera lachisanu kudzamvera State of the Nation Address (SONA) yomwe a mtsogoleri wa dziko Lazarus Chakwera anapeleka. A Chaponda ati… ...

Chelsea yakunthidwa
Malawi News

Chelsea yakunthidwa

Usiku wa dzulo Brighton yalongosola nsagwada za Chelsea pozipinda katatu pa bwalo la Falmer mu chikho cha English Premier League (EPL) komwe Chelsea inali alendo. Kaoru Mitoma anakhazika chete Chelsea asanabwere Yonkuba Minteh ndi dzilango… ...

FAM to unveil Pasuwa today as MNCS bow down to Sports Ministry’s pressure
Malawi News

FAM to unveil Pasuwa today as MNCS bow down to Sports Ministry’s pressure

The Football Association of Malawi (FAM) is set to announce the hiring of former FCB Nyasa Big Bullets head coach Kalisto Pasuwa this afternoon at Mpira Village in Chiwembe. This follows a decision by the… ...

Awanjata akusakasaka msika wa Nyanga ya Njovu
Malawi News

Awanjata akusakasaka msika wa Nyanga ya Njovu

Apolisi m'boma la Nsanje atsekera matate atatu mchitolokosi atapezeka ndi Nyanga ya Njovu yomwe anatangwanika kutsatsa kufuna kupeza msika. Malinga ndi oyankhulira polisi m'bomali, a Agnese Zalakoma, omwe atsimikiza za nkhaniyi, atatuwa amangidwa nzika zakufuna… ...

Mayi wamangidwa chifukwa chopha mayi ake ndi hamala
Malawi News

Mayi wamangidwa chifukwa chopha mayi ake ndi hamala

Mayi Malita Kalirani a dzaka 66 awakwidzinga chifukwa chowaganizira kuti apha amayi awo a Nadimba Kalirani a zaka 82 powaphwanya ndi hamala ku Dowa. M'neneli wa apolisi m'boma la Dowa, a Alice Sitima watsimikiza nkhaniyi… ...

Tilandileni tafikanso, Blue Eagles yabweleranso mu TNM Super League
Malawi News

Tilandileni tafikanso, Blue Eagles yabweleranso mu TNM Super League

Itatuluka mu ligi m'chaka cha 2023, timu ya apolisi ya Blue Eagles tsopano yabweleranso mu ligi yayikulu ya mdziko muno ya TNM Super League kutsatira kukhala akatswiri mu chikho cha Chipiku Stores Central Region Football… ...

Anjatidwa kamba koba njinga
Malawi News

Anjatidwa kamba koba njinga

Mchithunzi powona zitha kumawoneka ngati ndi yawo njinga koma ayi, a Dalitso Peter ali m'manja mwa apolisi ku Lilongwe chifukwa choba njinga yamoto komanso kusunga munthu wina mokakamiza. Oyankhulira polisi ya Lilongwe, a Hastings Chigalu,… ...

Chakwera walamula lipoti la ngozi ya ndege lipelekedwe ku maanja
Malawi News

Chakwera walamula lipoti la ngozi ya ndege lipelekedwe ku maanja

Mtsogoleri wa dziko lino a Lazarus Chakwera ati lipoti la zotsatira za kafukufuku wa ngozi ya ndege lipelekedwe kwa maanja okhudzidwa pofika lero Lachisanu. A Chakwera atinso kuyambira lolemba lipotili alitanthauzire mu zilankhulo zina za… ...