• Saturday July, 2025

Mphatso Khutcha Richard

Mphatso Khutcha Richard

Articles by Mphatso Khutcha Richard

Opikisana 13 pa President ku Malawi ndi chibwana chabe – Chaima
Malawi News

Opikisana 13 pa President ku Malawi ndi chibwana chabe – Chaima

M'modzi mwa akatswiri ozukutapo pa ndale a George Chaima ati m'mene dziko la Malawi lilili nkukhala ndi atsogoleri mpaka khumi ndi atatu (13) okapikisana pa mpando wa utsogoleri wa dziko ndi chibwana chabe chomwe Malawi… ...

Chotsani pa udindo nduna ya zachitetezo ndi mkulu wa apolisi – Kabambe
Malawi News

Chotsani pa udindo nduna ya zachitetezo ndi mkulu wa apolisi – Kabambe

Mtsogoleri wa chipani cha United Transformation Movement (UTM) a Dalitso Kabambe ati zomwe achita apolisi powonelera anthu achiwembu  akumenya mwankhanza anthu ochita ziwonetselo zachotsa chikhulupiliro cha aMalawi pa apolisi awo. Iwo ati wamkulu wa apolisi… ...

Opikisana pa mpando wa utsogoleri wa dziko asanamizire kuti Mulungu waatuma – Chaima
Malawi News

Opikisana pa mpando wa utsogoleri wa dziko asanamizire kuti Mulungu waatuma – Chaima

M'modzi mwa olankhulapo pa nkhani za ndale ndi ulamuliro wabwino, George Chaima wati onse amene akudzapikisana nawo pa mpando wa mtsogoleri wa dziko, asamanamizile kuti atumidwa ndi Mulungu, ponena kuti ngati atumidwa ndi Mulungu akuyenera… ...

Atupele Muluzi ndi DPP ubale wawora, polavula moto kuti Mutharika wakalamba
Malawi News

Atupele Muluzi ndi DPP ubale wawora, polavula moto kuti Mutharika wakalamba

Ubale wa chipani cha Democratic Progressive (DPP) ndi United Democratic Front (UDF) watekeseka ndipo atsirana mphepo pomwe mtsogoleri wa chipani cha UDF Atupele Muluzi watsindika kuti a Peter Mutharika akula ndipo akuyenera akapume. A Muluzi… ...

A Mutharika ndi a Kabambe sadakatengebe ma pepala ku bungwe la MEC
Malawi News

A Mutharika ndi a Kabambe sadakatengebe ma pepala ku bungwe la MEC

Atsogoleri a zipani za Democratic Progressive (DPP) ndi United Transformation Movement (UTM) ndi ena mwa atsogoleri amene sadakatengebe zikalata zawo zowonetsa chidwi kuti apikisana nawo mu masankho amene akubwera a pa 16 September. Malinga ndi… ...

Odya Zake to contest in September polls
Malawi News

Odya Zake to contest in September polls

Michael Usi, president of the newly registered Odya Zake Alibe Mlandu, has disclosed that the party is strong and that it will contest in the forthcoming presidential elections on 16 September 2025. Usi made his… ...

JB, AM snubs ‘pathways to progress hard talk’ to frustrate Nya-uyu
Malawi News

JB, AM snubs ‘pathways to progress hard talk’ to frustrate Nya-uyu

One of the country's comedians, transformational speaker, and social media influencer, Felistus Nya-uyu Ngwira, has expressed disappointment with the former head of state, Joyce Banda and UDF leader, Atupele Muluzi,  for defying availability to a… ...

A Joyce Chitsulo aikidwa m’manda
Malawi News

A Joyce Chitsulo aikidwa m’manda

Misozi umakana kuwuma pomwe anthu amapelekeza thupi la yemwe anali wachiwiri kwa nduna ya zamaboma ang'ono ndi chitukuko cha kumudzi a Joyce Chitsulo kukaliyika m'manda dzulo kumudzi kwawo ku Thambani m'boma la Mwanza. Ndi nkhope… ...

Joseph Kamwendo wavomeleza kuti Creck Sporting sinachite bwino
Malawi News

Joseph Kamwendo wavomeleza kuti Creck Sporting sinachite bwino

Yemwe anali mphunzitsi wa timu ya mu mzinda wa Lilongwe ya Creck Sporting Club, Joseph Kamwendo wati chigamulo chakuchotsedwa ntchito kwake n'chosadabwitsa chifukwa chiyambileni ligi chaka chino timuyi yakhala isakuchita bwino. Mphunzitsiyu yemwe anachotsedwa ntchito… ...

Increasing public debts crowding private sector in Malawi
Malawi News

Increasing public debts crowding private sector in Malawi

Malawi Confederation of Chambers Commence and Industry (MCCCI) president Wisely Phiri has disclosed that the increase in the level of public debts in the country is crowding the private sector in terms of accessing funds,… ...